Top Songs By Lawi
Lyrics
Kwawachera pa bwalo onena miseche
Inu muli kalikali mpakana zitheke
Akusintha ma shift kujeda
M'mawa mpaka madzulo
Nkuda ali m'magulu mpaka m'bandakucha
Kujeda (mpakana kuche)
Mayi wanga (mpakana zitheke)
(Mapeto ake), ayimba cha?
(Ayimba wizulo)
(mpakana kuche)
Mayi wanga (amayi mpakana zifewe)
(Mapeto ake), ayimba cha?
(Ayimba wizulo)
Muwaleke okonda zopingana
Adzingowona mutalandira madalitso
Muwaleke okonda zolondana
Adzingowona mutalandira madalitso
Kumati ndiye chokondwetsa ndi chani pano?
Muzakuvutika kwanga, mpaka pa bwalo
Chosonkhanila ndikuti mundijede basi
Koma mangani malamba muchezera pano
Anthu oyipa inu
Mpakana kuche
Mpakana zitheke
Mapeto ake ayimba wizulo
Muwaleke okonda zopingana
Adzingowona mutalandira madalitso
Muwaleke okonda zolondana
Adzingowona mutalandira madalitso
Onani Nyerere zipanga ma bwalo kugwirizana zotuta (zituta)
Zituta ndi khama usiku mpaka m'bandakucha
Kodi inu monga munthu mumatani?
Nanga mwapindula chani ndikunenana?
Mpakana kuche
Mpakana zitheke
Mapeto ake ayimba wizulo
Mpakana kuche
Amayi mpakana zifewe
Mapeto ake ayimba wizulo
Muwaleke okonda zopingana
Adzingowona mutalandira madalitso
Muwaleke...
Lyrics powered by www.musixmatch.com